Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndiyeno Ahitofeli anauza Abisalomu kuti: “Ndilole chonde, ndisankhe amuna 12,000 kuti ndithamangitse Davide lero usiku.+

  • Salimo 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Amadikirira anthu pamalo obisika ngati mkango pamalo ake obisalapo.+

      Amawadikirira+ kuti atenge mokakamiza munthu wosautsika.

      Amakulunga wosautsika mu ukonde wake ndi kumutenga mokakamiza.+

  • Mika 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anthu okhulupirika atha padziko lapansi, ndipo pakati pa anthu palibe munthu wowongoka mtima.+ Onse amadikirira anzawo kuti akhetse magazi.+ Aliyense amasaka m’bale wake ndi ukonde.+

  • Machitidwe 23:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kutacha, Ayuda anakonza chiwembu+ ndi kulumbira mwa kudzitemberera+ kuti sadya kapena kumwa kanthu kufikira atapha Paulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena