Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 11:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kunabwera Mwana wa munthu ndipo anali kudya ndi kumwa,+ koma anthu akunenabe kuti, ‘Taonani! Munthu wosusuka ndi wokonda kwambiri vinyo, bwenzi la okhometsa msonkho ndi ochimwa.’+ Mulimonsemo, nzeru imatsimikizirika kuti ndi yolungama chifukwa cha ntchito zake.”+

  • Mateyu 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa nthawi ina, Yesu anali kudutsa m’munda wa tirigu pa tsiku la sabata.+ Ophunzira ake anamva njala ndipo anayamba kubudula ngala za tirigu n’kumadya.+

  • Afilipi 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anthu onse adziwe kuti ndinu ololera.+ Ambuye ali pafupi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena