Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Khala chete pamaso pa Yehova,+

      Ndipo umuyembekezere ndi mtima wako wonse.+

      Usapse mtima ndi aliyense amene zinthu zikumuyendera bwino,+

      Munthu amene akukwaniritsa zolinga zake zoipa.+

  • Salimo 73:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Onani! Awa ndi anthu oipa, amene akukhala mosatekeseka mpaka kalekale.+

      Iwo achulukitsa chuma chawo.+

  • Malaki 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Panopa anthu odzikuza tikuwatcha odala.+ Komanso anthu ochita zoipa zinthu zikuwayendera bwino.+ Iwo ayesa Mulungu koma sakulandira chilango.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena