Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 21:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno Afilisiti+ anabwera kudzachita nkhondo ndi Isiraeli. Pamenepo Davide ndi atumiki ake anapita komweko n’kumenyana ndi Afilisiti, ndipo Davide anatopa.

  • Salimo 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mphamvu yanga yauma gwaa, ngati phale.+

      Lilime langa lamamatira kunkhama zanga,+

      Ndipo mwandikhazika m’fumbi la imfa.+

  • Salimo 90:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti masiku athu onse atha chifukwa cha mkwiyo wanu.+

      Zaka zathu zafika kumapeto ngati mpweya wotuluka m’mphuno pousa moyo.+

  • Salimo 102:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Moyo wanga utafika pachimake, anachepetsa mphamvu zanga,+

      Anafupikitsa masiku a moyo wanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena