Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 24:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Pokolola maolivi mwa kukwapula mitengo yake, usabwerere m’mbuyo kukaona ngati m’nthambi zake muli zipatso zotsala. Zimenezo zikhale za mlendo wokhala m’dziko lanu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye.+

  • Yesaya 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 M’dzikolo mudzangotsala zokunkha ngati mmene zimatsalira mumtengo wa maolivi akaugwedeza: pamwamba pa nthambi padzangokhala maolivi awiri kapena atatu akupsa. Panthambi zobala zipatso padzangokhala maolivi anayi kapena asanu okha,” akutero Yehova, Mulungu wa Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena