Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 72:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Padziko lapansi padzakhala tirigu wambiri.+

      Pamwamba pa mapiri padzakhala tirigu wochuluka.+

      Zokolola za mfumu zidzachuluka ngati mitengo ya ku Lebanoni,+

      Ndipo anthu ochokera mumzinda adzaphuka ngati udzu wa panthaka.+

  • Salimo 85:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Choonadi chidzaphuka padziko lapansi,+

      Ndipo chilungamo chidzayang’ana pansi kuchokera kumwamba.+

  • Salimo 85:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova nayenso adzapereka zinthu zabwino,+

      Ndipo dziko lathu lidzapereka zipatso zake.+

  • Salimo 104:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso kuti mutuluke vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu.+

      Amachita zonsezi kuti nkhope ya munthu isalale ndi mafuta,+

      Komanso kuti apereke chakudya chimene chimakhutiritsa mtima wa munthu.+

  • Yeremiya 31:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pamenepo iwo adzabwera ndi kufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+ Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa Yehova.+ Zidzawalanso chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano,+ mafuta, ana a nkhosa ndi ana a ng’ombe.+ Moyo wawo udzakhala ngati munda wothiriridwa bwino+ ndipo sadzakhalanso ofooka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena