Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Imvani mawu a Yehova,+ inu olamulira ankhanza+ a ku Sodomu.+ Mvetserani malamulo a Mulungu wathu, inu anthu a ku Gomora.

  • Yesaya 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Olamulira ako onse ankhanza+ athawa nthawi imodzi.+ Atengedwa ukaidi popanda kugwiritsa ntchito uta. Anthu ako onse amene apezeka atengedwa ukaidi limodzi.+ Iwo anali atathawira kutali.

  • Yohane 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho Yesu atadziwa kuti iwo akufuna kumugwira kuti amuveke ufumu, anachoka+ ndi kupitanso kuphiri yekhayekha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena