-
Zefaniya 2:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Magulu a nyama, nyama zakutchire za m’deralo zidzagona momasuka pakati pa mzindawo.+ Nungu ndiponso mbalame ya vuwo+ zidzagona usiku wonse pakati pa zipilala zakugwa za mzindawo.+ Pawindo padzamveka mawu a nyimbo. Pamakomo a nyumba padzakhala zibuma za nyumba zakugwa, pakuti iye adzakanganula matabwa oyalidwa kukhoma.*+
-