Salimo 86:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Pakuti inu ndinu wamkulu ndipo mukuchita zinthu zodabwitsa.+Inu nokha ndinu Mulungu.+ Yesaya 6:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Aliyense anali kuuza mnzake kuti: “Woyera, woyera, woyera ndiye Yehova wa makamu.+ Zonse zimene zili padziko lapansi zimasonyeza ulemerero wake.”
3 Aliyense anali kuuza mnzake kuti: “Woyera, woyera, woyera ndiye Yehova wa makamu.+ Zonse zimene zili padziko lapansi zimasonyeza ulemerero wake.”