-
Yobu 23:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Bwenzi nditapita pamaso pake ndi nkhani yoti aweruze.
M’kamwa mwanga bwenzi nditadzazamo mfundo zodziikira kumbuyo.
-
Yesaya 43:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Mitundu yonse isonkhanitsidwe pamalo amodzi, ndipo mitundu ya anthu ikhale pamodzi.+ Ndani pakati pawo amene anganene zimenezi?+ Kapena ndani amene angatiuze zinthu zimene zidzayambirire kuchitika?+ Abweretse mboni zawo+ kuti akhale olungama ndipo mbonizo zimve ndi kunena kuti, ‘Zimenezo ndi zoona!’”+
-
-
-