Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mudzawabweretsa ndi kuwakhazikitsa m’phiri limene ndi cholowa chanu.+

      Malo okhazikika amene mwakonzeratu kuti mukakhalemo,+ inu Yehova.

      Malo opatulika+ amene manja anu, inu Yehova, anakhazikitsa.

  • Salimo 147:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova amasangalala ndi anthu amene amamuopa,+

      Amene amayembekezera kukoma mtima kwake kosatha.+

  • Salimo 149:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti Yehova amasangalala ndi anthu ake.+

      Iye amakongoletsa anthu ofatsa ndi chipulumutso.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena