Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho Mika anati: “Tsopano ndadziwa kuti Yehova andichitira zabwino, chifukwa Mlevi wakhala wansembe wanga.”+

  • Yeremiya 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Chonde tifunsire kwa Yehova+ chifukwa Nebukadirezara mfumu ya Babulo akufuna kumenyana nafe nkhondo.+ Mwina Yehova adzatichitira imodzi mwa ntchito zake zamphamvu kuti Nebukadirezarayo atichokere.”+

  • Aroma 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsopano ngati ndiwe Myuda dzina lokha+ ndipo umadalira chilamulo+ ndi kunyadira Mulungu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena