Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 112:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Waunika mu mdima kuti anthu owongoka mtima aone kuwala.+

      ח [Chehth]

      Iye ndi wachisomo, wachifundo ndi wolungama.+

  • Yesaya 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anthu amene anali kuyenda mu mdima, aona kuwala kwakukulu.+ Anthu amene anali kukhala m’dziko la mdima wandiweyani,+ kuwala kwawawalira.+

  • Luka 1:79
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 79 ndipo kudzaunikira amene akhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa,+ ndi kutsogolera bwinobwino mapazi athu panjira yamtendere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena