Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 90:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mwawawonongeratu,+ ndipo amangozimiririka ngati maloto.+

      M’mawa amakhala ngati msipu wobiriwira umene watsitsimuka.+

  • Salimo 103:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Masiku a moyo wa munthu ali ngati masiku a udzu wobiriwira.+

      Iye amaphuka ngati mmene duwa lakutchire limaphukira.+

  • Yesaya 40:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tamvera! Winawake akunena kuti: “Lankhula mofuula!”+ Ndiye wina akuti: “Ndilankhule mofuula za chiyani?”

      “Anthu onse ali ngati udzu wobiriwira ndipo kukoma mtima kwawo konse kosatha kuli ngati maluwa akutchire.+

  • 1 Petulo 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pakuti “anthu onse ali ngati udzu, ndipo ulemerero wawo wonse uli ngati duwa la udzu.+ Udzuwo umafota ndipo duwalo limathothoka,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena