-
Salimo 30:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Mwasintha kulira kwanga kuti kukhale kuvina.+
Mwandivula chiguduli* changa ndipo mwandiveka chisangalalo,+
-
Yesaya 61:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 ndiponso kuti anthu onse amene akulirira Ziyoni ndiwapatse nsalu yovala kumutu m’malo mwa phulusa,+ ndiwapatse mafuta kuti azisangalala+ m’malo molira, ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda m’malo mokhala otaya mtima.+ Iwo adzatchedwa mitengo ikuluikulu ya chilungamo,+ yobzalidwa ndi Yehova+ kuti iyeyo akongole.+
-
-
-