Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 113:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Akuchititsa mkazi wosabereka kukhala m’nyumba+

      Monga mayi wosangalala wa ana aamuna.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Aroma 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mwa njira imeneyi, Aisiraeli onse+ adzapulumuka. Izi zikugwirizana ndi zimene Malemba amanena kuti: “Wolanditsa adzachokera m’Ziyoni+ ndi kuchotsera Yakobo zochita zonse zosalemekeza Mulungu.+

  • Agalatiya 3:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiponso ngati muli a Khristu, ndinudi mbewu ya Abulahamu,+ olandira cholowa mogwirizana ndi lonjezolo.+

  • Agalatiya 4:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma Yerusalemu+ wam’mwamba ndi mfulu, ndipo ndiye mayi wathu.+

  • Chivumbulutso 7:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno ndinamva chiwerengero cha amene anadindidwa chidindo. Anthu okwana 144,000,+ ochokera m’fuko lililonse+ la ana a Isiraeli,+ anadindidwa chidindo:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena