Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Yehova anaitananso kachitatu kuti: “Samueli!” Pamenepo Samueli anadzuka ndi kupita kwa Eli, n’kunenanso kuti: “Ndabwera, chifukwa mwandiitana ndithu.”

      Atatero, Eli anazindikira kuti Yehova ndi amene anali kuitana mwanayo.

  • Salimo 110:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Anthu ako+ adzadzipereka mofunitsitsa+ pa tsiku limene udzatsogolera asilikali ako kunkhondo.+

      Wadzikongoletsa ndi ulemerero,+

      Ndipo gulu la achinyamata amene ali ngati mame a m’bandakucha lili pamodzi ndi iwe.+

  • Mateyu 4:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Nthawi yomweyo iwo anasiya maukonde awo+ n’kumutsatira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena