Oweruza 5:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Posunga tsitsi lalitali mu Isiraeli monga lumbiro la nkhondo,Chifukwa cha kudzipereka mwaufulu kwa anthu,+Tamandani Yehova.+ Salimo 119:108 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 108 Inu Yehova, chonde kondwerani ndi nsembe zaufulu za pakamwa panga,+Ndipo ndiphunzitseni zigamulo zanu.+ Yesaya 6:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Kenako ndinayamba kumva mawu a Yehova akufunsa kuti: “Kodi nditumiza ndani, ndipo ndani apite m’malo mwa ife?”+ Ine ndinayankha kuti: “Ine ndilipo! Nditumizeni.”+ Mateyu 4:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Nthawi yomweyo iwo anasiya maukonde awo+ n’kumutsatira. Luka 5:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Pamenepo Leviyo anasiya chilichonse,+ ndipo ananyamuka n’kumutsatira. 1 Akorinto 9:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Ndikachita zimenezi mwaufulu,+ ndili ndi mphoto.+ Koma ndikachita motsutsana ndi kufuna kwanga, sindingachitire mwina, ndinebe woyang’anira mogwirizana ndi udindo+ umene unaikidwa m’manja mwanga.
2 “Posunga tsitsi lalitali mu Isiraeli monga lumbiro la nkhondo,Chifukwa cha kudzipereka mwaufulu kwa anthu,+Tamandani Yehova.+
108 Inu Yehova, chonde kondwerani ndi nsembe zaufulu za pakamwa panga,+Ndipo ndiphunzitseni zigamulo zanu.+
8 Kenako ndinayamba kumva mawu a Yehova akufunsa kuti: “Kodi nditumiza ndani, ndipo ndani apite m’malo mwa ife?”+ Ine ndinayankha kuti: “Ine ndilipo! Nditumizeni.”+
17 Ndikachita zimenezi mwaufulu,+ ndili ndi mphoto.+ Koma ndikachita motsutsana ndi kufuna kwanga, sindingachitire mwina, ndinebe woyang’anira mogwirizana ndi udindo+ umene unaikidwa m’manja mwanga.