Salimo 92:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Anthu obzalidwa m’nyumba ya Yehova,+M’mabwalo a Mulungu wathu,+ adzakula mosangalala. Mateyu 15:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Koma iye anayankha kuti: “Mbewu iliyonse imene sinabzalidwe ndi Atate wanga wakumwamba idzazulidwa.+
13 Koma iye anayankha kuti: “Mbewu iliyonse imene sinabzalidwe ndi Atate wanga wakumwamba idzazulidwa.+