Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akudalitse chifukwa cha zimene wachita,+ ndipo Yehova, Mulungu wa Isiraeli akufupe mokwanira.+ Iye amene m’mapiko mwake wathawiramo ndi kupezamo chitetezo.”+

  • Salimo 117:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti kukoma mtima kosatha kumene watisonyeza ndi kwakukulu.+

      Ndipo choonadi+ cha Yehova chidzakhalapobe mpaka kalekale.

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Zekariya 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndithu ndidzawabweretsa, ndipo adzakhala mu Yerusalemu.+ Iwo adzakhala anthu anga+ ndipo ine ndidzakhala Mulungu wawo woona ndi wachilungamo.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena