Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kefara-amoni, Ofini, ndi Geba.+ Mizinda 12 ndi midzi yake.

  • Yoswa 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kuchokera m’fuko la Benjamini, anawapatsa Gibeoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Geba+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • 2 Mbiri 16:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno mfumu Asa inatenga Ayuda onse,+ ndipo iwo anapita kukatenga miyala ya ku Rama+ ndi matabwa ake, zimene Basa ankamangira.+ Mfumuyo inatenga zinthu zimenezo n’kuyamba kukamangira Geba+ ndi Mizipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena