-
Zekariya 14:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 “Dziko lonse lidzasintha ndi kukhala ngati chigwa cha Araba+ kuyambira ku Geba+ kukafika ku Rimoni+ kum’mwera kwa Yerusalemu. Mzindawu udzakwezedwa pamalo ake ndipo anthu adzakhalamo.+ Anthuwo adzakhalamo kuyambira ku Chipata cha Benjamini+ mpaka ku Chipata Choyamba, kukafika ku Chipata cha Pakona. Komanso adzakhala kuyambira ku Nsanja ya Hananeli+ mpaka kukafika kumalo a mfumu oponderamo mphesa.
-