Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kefara-amoni, Ofini, ndi Geba.+ Mizinda 12 ndi midzi yake.

  • 1 Mbiri 6:60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 Kuchokera ku fuko la Benjamini, anawapatsa mzinda wa Geba+ ndi malo ake odyetserako ziweto, mzinda wa Alemeti+ ndi malo ake odyetserako ziweto, ndiponso mzinda wa Anatoti+ ndi malo ake odyetserako ziweto. Mizinda yonse ya mabanja awo inalipo 13.+

  • Yesaya 10:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Wadutsa powolokera mtsinje. Usiku agona ku Geba.+ Rama+ wanjenjemera ndipo Gibeya,+ kwawo kwa Sauli, wathawa.

  • Zekariya 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Dziko lonse lidzasintha ndi kukhala ngati chigwa cha Araba+ kuyambira ku Geba+ kukafika ku Rimoni+ kum’mwera kwa Yerusalemu. Mzindawu udzakwezedwa pamalo ake ndipo anthu adzakhalamo.+ Anthuwo adzakhalamo kuyambira ku Chipata cha Benjamini+ mpaka ku Chipata Choyamba, kukafika ku Chipata cha Pakona. Komanso adzakhala kuyambira ku Nsanja ya Hananeli+ mpaka kukafika kumalo a mfumu oponderamo mphesa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena