Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 106:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iye anangotsala pang’ono kulamula kuti awawononge,+

      Koma Mose wosankhidwa wake,

      Anaima pamalo ogumuka pamaso pa Mulungu,+

      Ndi kubweza mkwiyo wake kuti usawawononge.+

  • Ezekieli 22:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “‘Ndinafunafuna munthu pakati pawo amene angathe kukonzanso mpanda wamiyala+ ndi kuima pamalo ogumuka a mpandawo+ kuti ateteze dzikolo n’cholinga choti ine ndisaliwononge,+ koma sindinapeze aliyense.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena