Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “N’chifukwa chiyani tikungokhala? Sonkhanani pamodzi, ndipo tiyeni tilowe m’mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri+ kuti tikafere kumeneko. Pakuti Yehova Mulungu wathu watiweruza kuti tife,+ ndipo akutipatsa madzi apoizoni kuti timwe+ chifukwa tachimwira Yehova.

  • Yeremiya 35:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma pamene Nebukadirezara mfumu ya Babulo anabwera kudzaukira dzikoli+ tinati, ‘Tiyeni tilowe mu Yerusalemu chifukwa kukubwera magulu ankhondo a Akasidi ndi magulu ankhondo a ku Siriya. Tiyeni tikakhale mu Yerusalemu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena