Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Isimaeli anagwira anthu onse otsala, ana aakazi a mfumu,+ amene anali ku Mizipa.+ Anagwiranso anthu ena onse otsala ku Mizipa+ amene Nebuzaradani mkulu wa asilikali olondera mfumu anawapereka kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu+ kuti aziwayang’anira. Chotero Isimaeli mwana wa Netaniya anawagwira ndipo ananyamuka kuti awolokere nawo kudziko la ana a Amoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena