Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 32:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Tsopano ana a Gadi anayamba kumanga mizinda ya Diboni,+ Ataroti,+ Aroweli,+

  • Deuteronomo 2:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kuchokera ku Aroweli,+ mzinda umene uli m’mbali mwa chigwa cha Arinoni, ndiponso kuchokera kumzinda wa m’chigwa mpaka ku Giliyadi, panalibe mzinda womwe unali wa malinga aatali kwambiri kwa ife.+ Yehova Mulungu wathu anawapereka onsewo kwa ife.

  • 2 Samueli 24:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako anawoloka Yorodano ndi kumanga msasa ku Aroweli+ kudzanja lamanja la mzinda umene uli pakati pa chigwa,* kuyang’ana kudziko la Agadi+ ndi ku Yazeri.+

  • 1 Mbiri 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 ndi Bela. Bela anali mwana wa Azazi, Azazi anali mwana wa Sema, Sema anali mwana wa Yoweli.+ Bela anali kukhala m’dera loyambira ku Aroweli+ mpaka kukafika ku Nebo+ ndi ku Baala-meoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena