Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndidzathetsa phokoso lachikondwerero ndi phokoso lakusangalala m’malowo.+ Ndidzathetsanso mawu osangalala a mkwati ndi a mkwatibwi.+ Simudzamvekanso kupera kwa mphero+ ndipo simudzaonekanso kuwala kwa nyale.+

  • Yoweli 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kukondwera kwachoka pamaso pa ana a anthu.+ Ndithu mtengo wa mpesa wauma ndiponso mtengo wa mkuyu wafota. Mtengo wa makangaza* komanso mtengo wa kanjedza, mtengo wa maapozi ndi mitengo yonse yakuthengo yauma.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena