Yeremiya 50:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova, m’dzikomo simudzakhalanso anthu+ ndipo dziko lonselo lidzakhala bwinja.+ Aliyense wodutsa pafupi ndi Babulo adzayang’ana modabwa ndi kumuimbira mluzu chifukwa cha miliri yake yonse.+ Yeremiya 51:41 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 41 “Taonani! Sesaki walandidwa.+ Dziko lotamandidwa padziko lonse lapansi latengedwa.+ Babulo wakhala chinthu chodabwitsa pakati pa mitundu ya anthu.+ Chivumbulutso 18:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 ndipo azidzati, ‘Kalanga ine! Kalanga ine! Mzinda waukuluwe+ wovala zovala zapamwamba, zofiirira, ndi zofiira kwambiri. Mzinda wokongoletsedwa mochititsa kaso iwe, ndi zokongoletsera zagolide, zamwala wamtengo wapatali, ndi zangale.+
13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova, m’dzikomo simudzakhalanso anthu+ ndipo dziko lonselo lidzakhala bwinja.+ Aliyense wodutsa pafupi ndi Babulo adzayang’ana modabwa ndi kumuimbira mluzu chifukwa cha miliri yake yonse.+
41 “Taonani! Sesaki walandidwa.+ Dziko lotamandidwa padziko lonse lapansi latengedwa.+ Babulo wakhala chinthu chodabwitsa pakati pa mitundu ya anthu.+
16 ndipo azidzati, ‘Kalanga ine! Kalanga ine! Mzinda waukuluwe+ wovala zovala zapamwamba, zofiirira, ndi zofiira kwambiri. Mzinda wokongoletsedwa mochititsa kaso iwe, ndi zokongoletsera zagolide, zamwala wamtengo wapatali, ndi zangale.+