Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiyeno anakhala pansi kuti adye chakudya.+ Koma pamene anakweza maso, anaona gulu la apaulendo la Aisimaeli.+ Anali kuchokera ku Giliyadi, ndipo ngamila zawo zinali zitanyamula mafuta onunkhira a labidanamu ndi a basamu, komanso makungwa a utomoni wonunkhira.+ Apaulendowo anali kupita ku Iguputo.

  • Genesis 43:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno bambo awo Isiraeli anawauza kuti: “Chabwino, ngati ndi choncho,+ chitani izi: Tengani zinthu zamtengo wapatali za dziko lino m’matumba anu, mukam’patse munthuyo monga mphatso.+ Tengani mafuta a basamu+ pang’ono, uchi+ pang’ono, mafuta onunkhira a labidanamu, khungwa la utomoni wonunkhira,+ mtedza wa pisitasho, ndi zipatso za amondi.+

  • Yeremiya 46:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Iwe namwali, mwana wamkazi wa Iguputo,+ pita ku Giliyadi kuti ukatenge mafuta a basamu.+ Wachulukitsa njira zochiritsira zosathandiza koma sudzachiritsidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena