Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Samalani kuti munganene mumtima mwanu kuti, ‘Chuma ichi ndachipeza ndi mphamvu zanga ndi nyonga za dzanja langa.’+

  • Salimo 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Palibe mfumu imene inapulumuka chifukwa cha kukula kwa gulu lake lankhondo.+

      Munthu wamphamvu sapulumuka chifukwa cha kuchuluka kwa mphamvu zake.+

  • Danieli 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Mfumuyo inali kunena kuti:+ “Kodi uyu si Babulo Wamkulu amene ine ndamanga ndi mphamvu zanga zazikulu+ ndiponso ndi ulemerero wanga waukulu ndi cholinga chakuti kukhale nyumba yachifumu?”+

  • 1 Akorinto 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chotero pasakhale munthu wodzitama chifukwa cha anthu, popeza zinthu zonse ndi zanu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena