Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Hoseya 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Efuraimu akupitiriza kunena kuti, ‘Inetu ndalemeradi,+ ndapeza zinthu zamtengo wapatali.+ Palibe amene angapeze cholakwa chachikulu pa ntchito zanga zonse.’+

  • Habakuku 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 N’chifukwa chake mdaniyo amaperekera nsembe khoka lake ndipo amafukizira nsembe yautsi ukonde wake wophera nsomba. Iye amatero chifukwa chakuti amapeza chakudya chonona ndiponso chakudya chopatsa thanzi chifukwa cha khoka ndi ukonde wakewo.+

  • 1 Akorinto 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kodi akukupangitsa kukhala wosiyana+ ndi ena ndani? Inde, uli ndi chiyani chimene sunachite kulandira?+ Ndiye ngati unachita kulandira zinthu zimenezo,+ n’chifukwa chiyani ukudzitama+ ngati kuti sunachite kulandira?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena