Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 49:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ngakhale kuti panopa malo ako ndi owonongeka, osakazidwa ndiponso abwinja,+ ngakhale kuti panopa malo ako ndi osatakasuka mokwanira kuti n’kukhalamo bwinobwino, ndipo okumeza akhala kutali,+

  • Yeremiya 51:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 “Nebukadirezara mfumu ya Babulo wandidya.+ Wandisokoneza ndi kundisandutsa chiwiya chopanda kanthu. Wandimeza ngati chinjoka chachikulu.+ Wakhuta zinthu zanga zokoma ndipo wanditsukuluza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena