Salimo 78:64 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 64 Ansembe ake anagwa ndi lupanga,+Ndipo akazi awo amasiye sanalire.+ Mateyu 23:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 kuti magazi onse olungama okhetsedwa padziko lapansi abwere pa inu,+ kuyambira magazi a Abele+ wolungama+ mpaka magazi a Zekariya mwana wa Barakiya, amene inu munamupha pakati pa nyumba yopatulika ndi guwa lansembe.+
35 kuti magazi onse olungama okhetsedwa padziko lapansi abwere pa inu,+ kuyambira magazi a Abele+ wolungama+ mpaka magazi a Zekariya mwana wa Barakiya, amene inu munamupha pakati pa nyumba yopatulika ndi guwa lansembe.+