Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 39:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndinakhala chete.+ Sindinatsegule pakamwa panga,+

      Pakuti inu munachitapo kanthu.+

  • Yeremiya 15:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Sindinakhale pansi ndi gulu la anthu okonda kuchita nthabwala+ ndi kuyamba kusangalala nawo.+ Ndakhala pansi ndekhandekha chifukwa dzanja lanu lili pa ine,+ chifukwa mwandidzaza ndi mkwiyo.+

  • Maliro 3:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Kodi munthu angadandaulirenji+ chifukwa cha zotsatirapo za tchimo lake?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena