Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kodi mumenyedwanso pati+ mmene mukupitiriza kupandukamu?+ Mutu wanu uli ndi zilonda zokhazokha, ndipo mtima wanu wafooka.+

  • Yeremiya 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndagwidwa ndi chisoni chosatha.+ Mtima wanga wadwala.

  • Maliro 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kuipa kwawo konse kuonekere pamaso panu, ndipo muwalange+ koopsa.

      Muwalange koopsa monga mmene mwandilangira ine chifukwa cha machimo+ anga onse.

      Pakuti ndikuusa+ moyo kwambiri ndipo mtima wanga ukudwala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena