Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 27:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Zinthu zako zamtengo wapatali, zinthu zimene unasunga,+ katundu wako wamalonda,+ anthu okuyendetsa, anthu ogwira ntchito mwa iwe,+ anthu omata molumikizira matabwa ako,+ anthu ako okugulitsira malonda, amuna ako onse ankhondo+ amene ali mwa iwe ndiponso amene ali pakati pa anthu ako onse, adzamira pakati pa nyanja pa tsiku la kuwonongedwa kwako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena