-
Ezekieli 27:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Zinthu zako zamtengo wapatali, zinthu zimene unasunga,+ katundu wako wamalonda,+ anthu okuyendetsa, anthu ogwira ntchito mwa iwe,+ anthu omata molumikizira matabwa ako,+ anthu ako okugulitsira malonda, amuna ako onse ankhondo+ amene ali mwa iwe ndiponso amene ali pakati pa anthu ako onse, adzamira pakati pa nyanja pa tsiku la kuwonongedwa kwako.+
-