2 Samueli 14:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tonsefe tidzafa+ ndi kukhala ngati madzi otayika amene sawoleka. Koma Mulungu wakonza zinthu+ ndipo ali ndi zifukwa zothandiza kuti munthu wopitikitsidwa asapitirize kukhala wopitikitsidwa. Ezekieli 18:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 “‘Kodi ine ndimasangalala ndi imfa ya munthu aliyense wochimwa?+ Kodi sindisangalala kuti munthu wochimwayo abwerere kusiya njira zakezo ndi kukhalabe ndi moyo?’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa. Luka 15:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Choncho ndikukuuzani, kumakhala chisangalalo chochuluka kwa angelo a Mulungu chifukwa cha munthu mmodzi wochimwa amene walapa.”+ 1 Timoteyo 2:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 amene chifuniro chake n’chakuti anthu, kaya akhale a mtundu wotani,+ apulumuke+ ndi kukhala odziwa choonadi+ molondola.+
14 Tonsefe tidzafa+ ndi kukhala ngati madzi otayika amene sawoleka. Koma Mulungu wakonza zinthu+ ndipo ali ndi zifukwa zothandiza kuti munthu wopitikitsidwa asapitirize kukhala wopitikitsidwa.
23 “‘Kodi ine ndimasangalala ndi imfa ya munthu aliyense wochimwa?+ Kodi sindisangalala kuti munthu wochimwayo abwerere kusiya njira zakezo ndi kukhalabe ndi moyo?’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.
10 Choncho ndikukuuzani, kumakhala chisangalalo chochuluka kwa angelo a Mulungu chifukwa cha munthu mmodzi wochimwa amene walapa.”+
4 amene chifuniro chake n’chakuti anthu, kaya akhale a mtundu wotani,+ apulumuke+ ndi kukhala odziwa choonadi+ molondola.+