Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 40:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 M’masomphenya a Mulungu, iye ananditengera m’dziko la Isiraeli ndi kundikhazika paphiri lalitali kwambiri.+ Mbali ya kum’mwera paphiripo panali chinachake chooneka ngati mzinda.+

  • Ezekieli 41:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndiyeno munthu uja ananditengera m’kachisi.* Mmenemo anayamba kuyeza zipilala zam’mbali. Chipilala china chinali mbali ya kumanzere ndipo china mbali ya kudzanja lamanja. Chipilala chilichonse chinali mikono 6 m’lifupi. Umenewu ndiwo unali muyezo wa chipilala chilichonse m’lifupi mwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena