Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anagawira cholowacho mafuko 9 ndi hafu, mwa kuchita maere,+ monga mmene Yehova analamulira kudzera mwa Mose.+

  • Ezekieli 47:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mugawane dzikoli kuti likhale cholowa chanu+ ndi cha alendo okhala pakati panu, amene abereka ana pakati panu.+ Alendowo akhale ngati nzika pakati pa ana a Isiraeli. Iwo apatsidwe cholowa pamodzi ndi inu pakati pa mafuko a Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena