Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 41:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Felemu la pakhomo la kachisi linali lofanana mbali zonse,+ ndipo kutsogolo kwa malo oyera kunali kuoneka motere:

  • Ezekieli 46:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mtsogoleri wa anthu azilowa kuchokera panja n’kufika pakhonde la kanyumba ka pachipata+ ndipo aziima pafupi ndi felemu la chipatacho.+ Ndiyeno ansembe azimuperekera nsembe yopsereza yathunthu ndi nsembe zake zachiyanjano. Mtsogoleriyo azigwada ndi kuwerama pakhomo la kanyumba ka pachipata,+ kenako azituluka koma chipatacho chisamatsekedwe kufikira madzulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena