Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno anapanga guwa lansembe lamkuwa.+ Guwalo linali lalikulu mikono 20 m’litali, mikono 20 m’lifupi ndipo kuchokera pansi kufika pamwamba linali lalitali mikono 10.+

  • 2 Mbiri 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Solomo anapatula+ malo a pakati pa bwalo la nyumba ya Yehova, chifukwa pamenepo anaperekerapo nsembe zopsereza,+ ndi mafuta a nsembe zachiyanjano. Anatero popeza guwa lansembe lamkuwa+ limene iye anamanga linachepa, ndipo sipakanakwana nsembe yopsereza, nsembe yambewu,+ ndi mafuta oundana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena