Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 38:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anapanganso nyanga+ m’makona ake anayi. Nyanga zakezo zinatuluka m’makona akewo, ndipo guwalo analikuta ndi mkuwa.+

  • 1 Mafumu 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Tsopano Solomo anaimirira kutsogolo kwa guwa lansembe+ la Yehova pamaso pa mpingo wonse wa Isiraeli. Kenako anatambasula manja ake n’kuwakweza kumwamba.+

  • 2 Mafumu 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano guwa lansembe+ lamkuwa limene linali pamaso pa Yehova, Ahazi analichotsa kutsogolo kwa nyumbayo. Analichotsa pakati pa guwa lansembe latsopano ndi nyumba ya Yehova,+ n’kuliika kumpoto kwa guwa lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena