Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iye anandiuza kuti: “Iwe mwana wa munthu, takweza maso ako uyang’ane kumpoto.” Chotero ndinakweza maso anga n’kuyang’ana kumpoto, ndipo ndinaona kuti kumpoto kwa chipata cha guwa lansembe kunali chizindikiro choimira nsanje+ pakhomo la chipatalo.

  • Ezekieli 37:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno anandifunsa kuti: “Iwe mwana wa munthu, kodi mafupa awa angakhale ndi moyo?” Pamenepo ndinayankha kuti: “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, ndinu amene mukudziwa bwino zimenezo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena