Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 24:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Abambo asaphedwe chifukwa cha machimo a ana, ndipo ana asaphedwe chifukwa cha machimo a abambo.+ Aliyense aziphedwa chifukwa cha tchimo lake.+

  • 2 Mafumu 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma ana a anthu akuphawo sanawaphe, mogwirizana ndi zimene zinalembedwa m’buku la chilamulo cha Mose chimene Yehova analamula. Iye analamula kuti:+ “Abambo asaphedwe chifukwa cha machimo a ana, ndipo ana asaphedwe chifukwa cha machimo a abambo. Aliyense aziphedwa chifukwa cha tchimo lake.”+

  • Yeremiya 31:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Koma munthu aliyense adzafa chifukwa cha zolakwa zake.+ Mano a munthu aliyense wodya mphesa yosapsa ndiwo adzayayamira.”

  • Ezekieli 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tamverani! Miyoyo yonse ndi yanga.+ Moyo+ wa bambo komanso moyo wa mwana, yonse ndi yanga.+ Moyo umene ukuchimwawo+ ndi umene udzafe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena