29 Ndipo taonani! pobweretsa tsoka, ndiyamba ndi mzinda wotchedwa ndi dzina langa.+ Kodi inuyo mukufuna kuti musalandire chilango?”’+
“‘Chilangochi sichikuphonyani pakuti ndikuitana lupanga kuti liukire anthu onse okhala padziko lapansi,’ watero Yehova wa makamu.