Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndikwera pamwamba pamalo okwezeka a m’mitambo.+ Ndidzipanga kukhala wofanana ndi Wam’mwambamwamba.’+

  • Danieli 8:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chifukwa cha kuzindikira kwake idzathadi kugwiritsa ntchito chinyengo.+ Idzadzitukumula kwambiri mumtima mwake,+ ndipo idzawononga anthu ambiri pa nthawi imene zinthu zikuiyendera bwino.+ Mfumuyo idzalimbana ndi Kalonga wa akalonga,+ ndipo idzathyoledwa koma osati ndi dzanja la munthu.+

  • 2 Atesalonika 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iye ndi wotsutsa+ amene amadzikweza pamwamba pa aliyense wotchedwa “mulungu” kapena chilichonse chopembedzedwa, moti amakhala pansi m’kachisi wa Mulungu, n’kumadzionetsera ngati mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena