-
Deuteronomo 32:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+
Moti anadya zokolola za m’minda.+
Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+
Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+
-
Luka 15:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 “Nzeru zitam’bwerera, anati, ‘Komatu aganyu ambiri a bambo ali ndi chakudya chochuluka, koma ine kuno ndikufa ndi njala!
-
-
-