Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 21:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kodi iwo amakhala ngati udzu wouluzika ndi mphepo?+

      Kapena ngati mankhusu* ouluka ndi mphepo yamkuntho?

  • Salimo 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma oipa sali choncho.

      Iwo ali ngati mankhusu* amene amauluzika ndi mphepo.+

  • Danieli 2:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Pamenepo chitsulo, dongo, mkuwa, siliva ndi golide, zonsezi zinaphwanyikaphwanyika ndipo zinakhala ngati mankhusu* apamalo opunthirapo mbewu+ m’chilimwe. Mphepo inaziuluza moti sizinaonekenso.+ Koma mwala umene unamenya chifanizirocho unakhala phiri lalikulu ndipo linadzaza dziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena