Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndipo mu ukulu wanu wopambana mumagwetsa otsutsana nanu.+

      Mumatulutsa mkwiyo wanu woyaka moto, ndipo umanyeketsa otsutsana nanu ngati mapesi.+

  • Salimo 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma oipa sali choncho.

      Iwo ali ngati mankhusu* amene amauluzika ndi mphepo.+

  • Salimo 35:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Akhale ngati mankhusu ouluzika ndi mphepo,+

      Mngelo wa Yehova awapitikitse.+

  • Yesaya 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mitundu ya anthu+ idzasokosera ngati mkokomo wa madzi ambiri. Iye adzawadzudzula,+ ndipo iwo adzathawira kutali. Adzathamangitsidwa ngati mankhusu* ouluzika ndi mphepo m’mapiri ndiponso adzauluzika ngati tizitsotso touluzika ndi mphepo yamkuntho.+

  • Hoseya 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chotero iwo adzakhala ngati mitambo ya m’mawa+ ndiponso ngati mame amene sachedwa kuuma. Adzakhalanso ngati mankhusu* amene amauluzika kuchokera pamalo opunthira mbewu+ ndiponso ngati utsi umene umatuluka m’chumuni kudenga.*

  • Mateyu 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Fosholo yake youluzira mankhusu* ili m’manja mwake, ndipo malo ake opunthirapo mbewu adzawayeretseratu kuti mbee! Tirigu adzamututira m’nkhokwe,+ koma mankhusu adzawatentha+ ndi moto umene sungazimitsidwe.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena