Yeremiya 13:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mizinda ya kum’mwera yatsekedwa moti palibe amene akuitsegula. Yuda yense watengedwa kupita ku ukapolo. Watengedwa wathunthu kupita ku ukapolo.+ Yeremiya 33:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 “Yehova wanena kuti, ‘Ziweto zidzadutsa pansi pa dzanja la munthu woziwerenga+ m’mizinda ya m’madera amapiri, m’mizinda ya m’chigwa,+ m’mizinda ya kum’mwera,+ m’dziko la Benjamini,+ m’madera ozungulira Yerusalemu+ ndi m’mizinda ya Yuda.’”+
19 Mizinda ya kum’mwera yatsekedwa moti palibe amene akuitsegula. Yuda yense watengedwa kupita ku ukapolo. Watengedwa wathunthu kupita ku ukapolo.+
13 “Yehova wanena kuti, ‘Ziweto zidzadutsa pansi pa dzanja la munthu woziwerenga+ m’mizinda ya m’madera amapiri, m’mizinda ya m’chigwa,+ m’mizinda ya kum’mwera,+ m’dziko la Benjamini,+ m’madera ozungulira Yerusalemu+ ndi m’mizinda ya Yuda.’”+